Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepo iwo anati: “Choka apa!” Ananenanso kuti: “Uyu ndi wobwera kwathu kuno, ndipo akukhala monga mlendo.+ Ndiye lero azitiuza zochita?+ Tsopano iweyo tikuchita zoopsa kuposa iwowo.” Atatero iwo anamukhamukira Lotiyo ndi kumupanikiza,+ moti anatsala pang’ono kuthyola chitseko.+

  • Ezekieli 33:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndikauza munthu woipa kuti, ‘Munthu woipa iwe, udzafa ndithu,’+ koma iwe osanena mawu alionse ochenjeza woipayo kuti asiye njira yake,+ iyeyo poti ndi woipa adzafa chifukwa cha zolakwa zake,+ koma magazi ake ndidzawafuna kuchokera m’manja mwako.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena