Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 41:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mukatero ndidziwa kuti mwasangalala nane,

      Chifukwa mdani wanga sadzafuula mosangalala kuti wandipambana.+

  • Salimo 84:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mphamvu zawo zidzapitiriza kuwonjezeka pamene akuyenda.+

      Aliyense wa iwo amaonekera kwa Mulungu mu Ziyoni.+

  • Miyambo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba.+ Wolungama amathawira mmenemo ndipo amatetezedwa.+

  • Yesaya 40:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 koma anthu odalira+ Yehova adzapezanso mphamvu.+ Iwo adzaulukira m’mwamba ngati ali ndi mapiko a chiwombankhanga.+ Adzathamanga koma osafooka. Adzayenda koma osatopa.”+

  • Afilipi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pa zinthu zonse, ndimapeza mphamvu kuchokera kwa iye amene amandipatsa mphamvu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena