Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 140:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Munthu wolankhula zazikulu* asakhazikike padziko lapansi.+

      Zoipa zisakesake munthu wochita zachiwawa ndipo zimukanthe mobwerezabwereza.+

  • Miyambo 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti amadya mkate wa zoipa+ ndipo amamwa vinyo wachiwawa.+

  • Habakuku 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chifukwa chakuti iwe unafunkha mitundu yambiri ya anthu, anthu onse otsala a m’mitunduyo adzafunkha zinthu zako.+ Iwo adzateronso chifukwa unakhetsa magazi a mtundu wa anthu komanso unachitira chiwawa dziko lapansi, tauni ndi anthu onse okhala mmenemo.+

  • Chivumbulutso 16:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 pakuti iwo anakhetsa magazi a oyera ndi a aneneri.+ Ndipo inu mwawapatsa magazi+ kuti amwe, ndipo n’zowayenereradi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena