Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kenako Yehova Mulungu anati: “Si bwino kuti munthu akhale yekha. Ndimupangira womuthandiza, monga mnzake womuyenerera.”+

  • 1 Samueli 23:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Tsopano Yonatani mwana wa Sauli ananyamuka ndi kupita kwa Davide ku Horesi, kuti akalimbikitse+ Davide kudalira Mulungu.+

  • Miyambo 27:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chitsulo chimanola chitsulo chinzake. Momwemonso munthu amanola munthu mnzake.+

  • Machitidwe 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pamene anali kutumikira+ Yehova ndi kusala kudya, mzimu woyera unati: “Mwa anthu onse, mundipatulire Baranaba ndi Saulo+ kuti agwire ntchito imene ndinawaitanira.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena