Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Atatero, anamuuza Yerobowamu kuti:

      “Tengapo zidutswa 10, pakuti Yehova Mulungu wa Isiraeli wati, ‘Ndikung’amba ufumuwu kuuchotsa m’manja mwa Solomo, ndipo iwe ndidzakupatsa mafuko 10.+

  • 1 Mafumu 11:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Masiku onse amene Solomo analamulira Isiraeli yense ku Yerusalemu anakwana zaka 40.+

  • Mlaliki 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Mawu a wosonkhanitsa anthu,+ mwana wa Davide, mfumu ya ku Yerusalemu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena