Yesaya 32:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pakuti nsanja yokhalamo yasiyidwa,+ piringupiringu amene anali mumzindamo watha. Ofeli+ ndi nsanja ya mlonda zasanduka tchire. Mpaka kalekale zidzakhala malo osangalalako mbidzi, ndi odyetserako ziweto, Yeremiya 9:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Yerusalemu ndidzamusandutsa milu ya miyala+ ndiponso malo obisalamo mimbulu.+ Mizinda ya Yuda ndidzaisandutsa mabwinja, malo opanda wokhalamo.+ Maliro 1:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Njira zopita ku Ziyoni zikulira, chifukwa palibe amene akupita kuchikondwerero.+Zipata zake zonse zasiyidwa.+ Ansembe+ ake akuusa moyo.*Anamwali ake agwidwa ndi chisoni,+ ndipo iyeyo akumva kuwawa mumtima. Maliro 2:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Zipata+ zake zamira munthaka. Wawononga mipiringidzo yake ndipo waithyolathyola.Mfumu yake ndi akalonga ake ali pakati pa mitundu ina.+ Malamulo sakutsatiridwa.+Aneneri ake sakuonanso masomphenya ochokera kwa Yehova.+ Mika 1:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Zilonda zake n’zosachiritsika+ ndipo zafalikira mpaka kukafika ku Yuda.+ Mliri umenewu wakafika pachipata cha anthu amtundu wanga ku Yerusalemu.+
14 Pakuti nsanja yokhalamo yasiyidwa,+ piringupiringu amene anali mumzindamo watha. Ofeli+ ndi nsanja ya mlonda zasanduka tchire. Mpaka kalekale zidzakhala malo osangalalako mbidzi, ndi odyetserako ziweto,
11 Yerusalemu ndidzamusandutsa milu ya miyala+ ndiponso malo obisalamo mimbulu.+ Mizinda ya Yuda ndidzaisandutsa mabwinja, malo opanda wokhalamo.+
4 Njira zopita ku Ziyoni zikulira, chifukwa palibe amene akupita kuchikondwerero.+Zipata zake zonse zasiyidwa.+ Ansembe+ ake akuusa moyo.*Anamwali ake agwidwa ndi chisoni,+ ndipo iyeyo akumva kuwawa mumtima.
9 Zipata+ zake zamira munthaka. Wawononga mipiringidzo yake ndipo waithyolathyola.Mfumu yake ndi akalonga ake ali pakati pa mitundu ina.+ Malamulo sakutsatiridwa.+Aneneri ake sakuonanso masomphenya ochokera kwa Yehova.+
9 Zilonda zake n’zosachiritsika+ ndipo zafalikira mpaka kukafika ku Yuda.+ Mliri umenewu wakafika pachipata cha anthu amtundu wanga ku Yerusalemu.+