Yesaya 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Dziko lawo ladzaza ndi milungu yopanda phindu.+ Iwo amagwadira ntchito ya manja awo. Amagwadira chinthu chimene zala zawo zapanga.+ Yesaya 30:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Zophimbira mafano anu ogoba asiliva ndi zokutira zifaniziro zanu zopangidwa ndi golide+ wosungunula,+ mudzaziona kuti ndi zonyansa+ ndipo mudzazitaya.+ Monga mkazi amene akusamba yemwe amataya monyansidwa kansalu kake, mudzanena kuti: “Nyansi zimenezi!”+ Yesaya 31:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pakuti m’tsiku limenelo, aliyense wa inu adzataya milungu yake yasiliva yachabechabe, ndi milungu yake yagolide yopanda phindu,+ imene manja anu akupangirani n’kukuchimwitsani nayo.+
8 Dziko lawo ladzaza ndi milungu yopanda phindu.+ Iwo amagwadira ntchito ya manja awo. Amagwadira chinthu chimene zala zawo zapanga.+
22 Zophimbira mafano anu ogoba asiliva ndi zokutira zifaniziro zanu zopangidwa ndi golide+ wosungunula,+ mudzaziona kuti ndi zonyansa+ ndipo mudzazitaya.+ Monga mkazi amene akusamba yemwe amataya monyansidwa kansalu kake, mudzanena kuti: “Nyansi zimenezi!”+
7 Pakuti m’tsiku limenelo, aliyense wa inu adzataya milungu yake yasiliva yachabechabe, ndi milungu yake yagolide yopanda phindu,+ imene manja anu akupangirani n’kukuchimwitsani nayo.+