Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti nyenyezi zakumwamba ndi magulu a nyenyezi a Kesili+ sizidzawala. Dzuwa lidzachita mdima potuluka, ndipo mwezi sudzaonetsa kuwala kwake.

  • Obadiya 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ngakhale malo ako atakhala pamwamba ngati a chiwombankhanga, kapena ngakhale utamanga chisa chako pakati pa nyenyezi, ine ndidzakugwetsa kuchokera pamenepo,”+ watero Yehova.

  • Obadiya 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kodi pa tsiku limenelo sindidzawononga anthu anzeru mu Edomu?”+ watero Yehova.

      “Ndiponso kodi sindidzawononga anthu ozindikira a m’dera lamapiri la Esau?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena