2 Mbiri 29:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Pa chifukwa chimenechi, makolo athu anaphedwa ndi lupanga+ ndipo ana athu aamuna ndi aakazi ndiponso akazi athu anapita ku ukapolo.+ Yeremiya 11:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Yehova wa makamu wanena kuti: “Tsopano ndikuwapatsa chilango. Anyamata adzafa ndi lupanga.+ Ana awo aamuna ndi aakazi adzafa ndi njala yaikulu.+ Maliro 2:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Anyamata ndi amuna okalamba+ agona pansi m’misewu.+Anamwali anga ndi anyamata anga aphedwa ndi lupanga.+Mwapha anthu pa tsiku la mkwiyo+ wanu. Onsewo mwawaphadi+ mopanda chisoni.+ Amosi 9:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Anthu anga onse ochimwa adzaphedwa ndi lupanga.+ Iwo amanena kuti: “Tsoka silitiyandikira kapena kutigwera.”’+
9 Pa chifukwa chimenechi, makolo athu anaphedwa ndi lupanga+ ndipo ana athu aamuna ndi aakazi ndiponso akazi athu anapita ku ukapolo.+
22 Yehova wa makamu wanena kuti: “Tsopano ndikuwapatsa chilango. Anyamata adzafa ndi lupanga.+ Ana awo aamuna ndi aakazi adzafa ndi njala yaikulu.+
21 Anyamata ndi amuna okalamba+ agona pansi m’misewu.+Anamwali anga ndi anyamata anga aphedwa ndi lupanga.+Mwapha anthu pa tsiku la mkwiyo+ wanu. Onsewo mwawaphadi+ mopanda chisoni.+
10 Anthu anga onse ochimwa adzaphedwa ndi lupanga.+ Iwo amanena kuti: “Tsoka silitiyandikira kapena kutigwera.”’+