Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 39:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Taonani! Mwachepetsa masiku anga.+

      Ndipo nthawi ya moyo wanga si kanthu pamaso panu.+

      Ndithudi, munthu aliyense ngakhale atakhala wamphamvu bwanji, sali kanthu koma ali ngati mpweya wotuluka m’mphuno.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 62:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndithudi, ana a anthu ochokera kufumbi ali ngati mpweya,+

      Ana a anthu ndi malo othawirako achinyengo.+

      Onse pamodzi akaikidwa pasikelo ndi opepuka kuposa mpweya.+

  • Danieli 4:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Iye amaona anthu onse okhala padziko lapansi ngati opanda pake+ ndipo amachita zinthu mogwirizana ndi chifuniro chake pakati pa makamu akumwamba ndi pakati pa anthu okhala padziko lapansi.+ Palibe aliyense amene angaletse dzanja+ lake kapena kumufunsa kuti, ‘Mukuchita chiyani?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena