Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 77:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Kodi Yehova watitaya mpaka kalekale?+

      Kodi sitidzathanso kumusangalatsa?+

  • Yesaya 49:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma Ziyoni ankangonena kuti: “Yehova wandisiya+ ndipo Yehova wandiiwala.”+

  • Yesaya 60:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “M’malo mokhala wosiyidwa mpaka kalekale ndi wodedwa, popanda aliyense wodutsa mwa iwe,+ ine ndidzakuika monga chinthu chonyaditsa mpaka kalekale, ndiponso chinthu chokondweretsa ku mibadwomibadwo.+

  • Ezekieli 37:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iye anandiuzanso kuti: “Iwe mwana wa munthu, mafupawa akuimira nyumba yonse ya Isiraeli.+ Iwo akunena kuti, ‘Mafupa athu auma ndipo tilibenso chiyembekezo chilichonse.+ Atilekanitsa ndi anzathu ndipo tili kwatokhatokha.’

  • Aroma 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiye ndifunse kuti, kodi Mulungu anakana anthu ake?+ Ayi ndithu! Paja inenso ndine Mwisiraeli,+ wa mbewu ya Abulahamu, wa fuko la Benjamini.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena