Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 27:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Pali Mulungu wamoyo+ amene wandimana chilungamo,+

      Ndiponso pali Wamphamvuyonse wamoyo amene wachititsa moyo wanga kupweteka,+

  • Yobu 34:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Pakuti Yobu wanena kuti, ‘Ndithu ine si ine wolakwa,+

      Koma Mulungu wapotoza chiweruzo changa.+

  • Luka 18:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndithu, ngakhale kuti Mulungu amalezera mtima+ osankhidwa ake, kodi sadzaonetsetsa kuti chilungamo+ chachitika kwa iwo, amene amafuulira kwa iye usana ndi usiku?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena