Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 71:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Kuyambira ndili m’mimba mwa mayi anga inu mwandithandiza.+

      Inu ndi amene munanditulutsa m’mimba mwa mayi anga.+

      Ndimatamanda inu nthawi zonse.+

  • Yesaya 49:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Ndimvereni zilumba inu,+ ndipo mvetserani, inu mitundu ya anthu akutali.+ Yehova anandiitana+ ndili m’mimba.+ Ndili mkati mwa mayi anga, anatchula dzina langa.+

  • Yeremiya 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Ndisanakuumbe m’mimba,+ ndinakudziwa,+ ndipo usanatuluke m’mimbamo, ndinakusankha kuti uchite ntchito yopatulika.+ Ndinakusankha kuti ukhale mneneri ku mitundu ya anthu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena