Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti woipa amadzitamandira ndi zilakolako zake zadyera,+

      Ndipo wopanga phindu lachinyengo+ amadzitamanda.

      נ [Nun]

      Iye amanyoza Yehova.+

  • Salimo 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Wopusa amanena mumtima mwake kuti:

      “Kulibe Yehova.”+

      Anthu oterewa amachita zoipa,+ ndipo amachita zinthu zonyansa.

      Palibe amene akuchita zabwino.+

  • Salimo 36:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mawu a pakamwa pake ndi opweteka ndi achinyengo.+

      Wasiya kugwiritsa ntchito nzeru zomuthandiza kuchita zinthu zabwino.+

  • Miyambo 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 mtima wokonzera ena ziwembu,+ mapazi othamangira kukachita zoipa,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena