Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 18:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pansi, mizu yake idzauma.+

      Pamwamba, nthambi yake idzafota.

  • Hoseya 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Efuraimu adzavulazidwa.+ Muzu wake udzauma,+ ndipo sadzaberekanso chipatso chilichonse.+ Komanso ngati angabereke, ndidzapha chipatso chokondedwa cha mimba yawo.”+

  • Amosi 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “‘Koma ine ndinawononga Aamori+ chifukwa cha anthu anga. Aamoriwo misinkhu yawo inali yofanana ndi mitengo ya mkungudza ndipo mphamvu zawo zinali zofanana ndi za mitengo ikuluikulu.+ Ndinawononga zipatso zawo m’mwamba ndiponso mizu yawo pansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena