Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Tsopano anthu odutsa anayamba kunena mawu onyoza+ Yesu. Anali kupukusa+ mitu yawo

  • Mateyu 27:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Chimodzimodzinso ansembe aakulu limodzi ndi alembi komanso akulu. Nawonso anayamba kum’chita chipongwe ndi kunena kuti:+

  • Yohane 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tsopano Pilato anatenga Yesu ndi kumukwapula.+

  • 1 Petulo 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamene anali kunenedwa zachipongwe,+ sanabwezere zachipongwe.+ Pamene anali kuvutika,+ sanawopseze, koma anali kudzipereka kwa iye+ amene amaweruza molungama.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena