Mateyu 19:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Pakuti ena sakwatira chifukwa chakuti anabadwa choncho kuchokera m’mimba mwa mayi awo,+ ndipo ena chifukwa chakuti anafulidwa ndi anthu. Koma pali ena amene safuna kukwatira chifukwa cha ufumu wakumwamba. Amene angathe kuchita zimenezi achite.”+ 1 Akorinto 7:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Nayenso amene walekana ndi moyo wokhala yekha* n’kulowa m’banja wachita bwino,+ koma amene sanalowe m’banja wachita bwino koposa.+ 2 Akorinto 5:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Ndiye chifukwa chake kuyambira tsopano sitiona munthu mwakuthupi.+ Ngakhale kuti Khristu tinamuona mwakuthupi,+ tsopano sitikumuonanso motero.+
12 Pakuti ena sakwatira chifukwa chakuti anabadwa choncho kuchokera m’mimba mwa mayi awo,+ ndipo ena chifukwa chakuti anafulidwa ndi anthu. Koma pali ena amene safuna kukwatira chifukwa cha ufumu wakumwamba. Amene angathe kuchita zimenezi achite.”+
38 Nayenso amene walekana ndi moyo wokhala yekha* n’kulowa m’banja wachita bwino,+ koma amene sanalowe m’banja wachita bwino koposa.+
16 Ndiye chifukwa chake kuyambira tsopano sitiona munthu mwakuthupi.+ Ngakhale kuti Khristu tinamuona mwakuthupi,+ tsopano sitikumuonanso motero.+