Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 44:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti iwo sanatenge dzikolo chifukwa cha lupanga lawo,+

      Ndipo si mkono wawo umene unawabweretsera chipulumutso.+

      Koma chinabwera ndi dzanja lanu lamanja,+ mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu,

      Chifukwa munakondwera nawo.+

  • Salimo 98:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 98 IMBIRANI Yehova nyimbo yatsopano,+

      Pakuti zimene wachita ndi zodabwitsa.+

      Dzanja lake lamanja, ndithu mkono wake woyera, wabweretsa chipulumutso.+

  • Yesaya 51:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Dzuka! Dzuka! Vala mphamvu,+ iwe dzanja la Yehova!+ Dzuka ngati masiku akale, ngati m’mibadwo yakalekale.+ Kodi si iwe amene unaphwanyaphwanya Rahabi,+ amene unabaya* chilombo cha m’nyanja?+

  • Yesaya 52:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehova waika pamtunda dzanja lake loyera kuti mitundu yonse ione,+ ndipo malekezero onse a dziko lapansi adzaona chipulumutso cha Mulungu wathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena