Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma ndimasonyeza kukoma mtima kosatha ku mibadwo masauzande chifukwa cha anthu amene amandikonda ndi kusunga malamulo anga.+

  • Salimo 63:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti kukoma mtima kwanu kosatha n’kwabwino kuposa moyo,+

      Milomo yanga idzakuyamikirani.+

  • Salimo 107:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anthu ayamike Yehova chifukwa cha kukoma mtima kwake kosatha,+

      Ndiponso chifukwa cha ntchito zake zodabwitsa zimene wachitira ana a anthu.+

  • Salimo 136:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 136 Yamikani Yehova anthu inu, pakuti iye ndi wabwino:+

      Kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena