Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Chonde kumbukirani kuti munandiumba ndi dongo,+

      Ndipo mudzandibwezera kufumbi.+

  • Yesaya 29:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu inu ndinu opotoka maganizo kwabasi! Kodi woumba zinthu ndi dongo angafanane ndi dongolo?+ Kodi chinthu chochita kupangidwa chingamunene amene anachipanga, kuti: “Iye uja sanandipange”?+ Komanso kodi chinthu chochita kuumbidwa chingamunene amene anachiumba, kuti: “Iye uja sanasonyeze kuti ndi womvetsa zinthu”?+

  • Yeremiya 18:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “‘Anthu inu, kodi sindingathe kukuchitirani mofanana ndi mmene woumba mbiyayu anachitira, inu nyumba ya Isiraeli?’ watero Yehova. ‘Taonani! Mofanana ndi dongo limene lili m’manja mwa woumba mbiya, ndi mmene inunso mulili kwa ine, inu nyumba ya Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena