Yesaya 34:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Anthu awo ophedwa adzatayidwa, ndipo fungo loipa la mitembo yawo lidzakwera m’mwamba.+ Mapiri adzasungunuka chifukwa cha magazi awo.+ Yeremiya 15:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “‘Ndidzawagwetsera masoka a mitundu inayi,’+ watero Yehova. ‘Ndidzawatumizira lupanga kuti liwaphe, agalu kuti akoke mitembo yawo, zolengedwa zouluka zam’mlengalenga+ ndi zilombo zakutchire kuti ziwadye ndi kuwawononga. Ezekieli 32:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndidzakusiya pamtunda ndiponso ndidzakuponya kuchigwa.+ Ndidzachititsa kuti zolengedwa zonse zouluka m’mlengalenga zitere pa iwe. Ndidzakhutitsa zilombo zakutchire ndi nyama yako.+ Chivumbulutso 19:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Ndinaonanso mngelo ataimirira padzuwa. Iye anafuula ndi mawu okweza kwa mbalame+ zonse zouluka chapafupi m’mlengalenga, kuti: “Bwerani kuno, dzasonkhaneni ku phwando lalikulu la Mulungu la chakudya chamadzulo,
3 Anthu awo ophedwa adzatayidwa, ndipo fungo loipa la mitembo yawo lidzakwera m’mwamba.+ Mapiri adzasungunuka chifukwa cha magazi awo.+
3 “‘Ndidzawagwetsera masoka a mitundu inayi,’+ watero Yehova. ‘Ndidzawatumizira lupanga kuti liwaphe, agalu kuti akoke mitembo yawo, zolengedwa zouluka zam’mlengalenga+ ndi zilombo zakutchire kuti ziwadye ndi kuwawononga.
4 Ndidzakusiya pamtunda ndiponso ndidzakuponya kuchigwa.+ Ndidzachititsa kuti zolengedwa zonse zouluka m’mlengalenga zitere pa iwe. Ndidzakhutitsa zilombo zakutchire ndi nyama yako.+
17 Ndinaonanso mngelo ataimirira padzuwa. Iye anafuula ndi mawu okweza kwa mbalame+ zonse zouluka chapafupi m’mlengalenga, kuti: “Bwerani kuno, dzasonkhaneni ku phwando lalikulu la Mulungu la chakudya chamadzulo,