Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Adzakhala ngati mtengo umene uli pawokhawokha m’chipululu ndipo zabwino zikadzafika sadzatha kuziona.+ Iye adzakhala m’malo ouma a m’chipululu m’dziko la nthaka yamchere, kumene sikukhala anthu.+

  • Ezekieli 17:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Ndiyeno unene kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Kodi mtengo umenewu zinthu zidzauyendera bwino?+ Kodi munthu wina sadzadula mizu yake+ ndi kuwononga zipatso zake? Kodi mphukira zake zimene zangothyoledwa kumene sizidzauma?+ Mtengowo udzauma ndithu. Sudzachita kufuna dzanja lamphamvu kapena anthu ambiri kuti uzulidwe ndi mizu yomwe.

  • Mateyu 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kenako anaona mkuyu m’mbali mwa msewu ndipo atapita pomwepo, sanapezemo chilichonse+ koma masamba okhaokha. Choncho anauza mtengowo kuti: “Kuyambira lero sudzabalanso zipatso kwamuyaya.”+ Ndipo mkuyuwo unafota nthawi yomweyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena