Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 35:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Njira yawo ikhale ya mdima ndi yoterera,+

      Ndipo mngelo wa Yehova aziwathamangitsa.

  • Salimo 73:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndithudi, mwawaimika pamalo oterera.+

      Mwawagwetsa kuti awonongeke.+

  • Miyambo 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Njira ya oipa ili ngati mdima.+ Iwo sadziwa chimene chimawapunthwitsa.+

  • Yeremiya 13:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Patsani Yehova Mulungu wanu ulemerero+ asanachititse mdima,+ komanso mapazi anu asanapunthwe pamapiri madzulo dzuwa litalowa.+ Mudzayembekeza kuwala+ koma iye adzabweretsa mdima,+ ndipo adzachititsa mdima wandiweyani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena