Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 48:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma Isiraeli anatambasula dzanja lake lamanja n’kuliika pamutu pa Efuraimu,+ ngakhale kuti ndiye anali wamng’ono.+ Anatambasulanso dzanja lake lamanzere n’kuliika pamutu pa Manase.+ Anasemphanitsa dala choncho manja ake chifukwa Manase ndiye anali mwana woyamba.+

  • Ekisodo 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Choncho ukamuuze Farao kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Isiraeli ndi mwana wanga wamwamuna, mwana wanga woyamba kubadwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena