Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 27:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Amuna a ku Perisiya,+ ku Ludi+ ndi ku Puti+ anali m’gulu lako lankhondo, anali m’gulu la asilikali ako. Amuna amenewa anali kupachika zishango ndi zisoti mwa iwe.+ Iwo ndi amene anakuchititsa kukhala waulemerero.

  • Ezekieli 38:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Udzabwera pamodzi ndi asilikali a ku Perisiya,+ Itiyopiya+ ndi Puti.+ Onsewa adzanyamula zishango zazing’ono ndipo adzavala zisoti.

  • Nahumu 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mphamvu zake zonse zinali kuchokera ku Itiyopiya komanso ku Iguputo,+ ndipo zinali zopanda malire. Anthu a ku Puti komanso a ku Libiya anali kumuthandiza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena