Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 11:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yehova wa makamu wanena kuti: “Tsopano ndikuwapatsa chilango. Anyamata adzafa ndi lupanga.+ Ana awo aamuna ndi aakazi adzafa ndi njala yaikulu.+

  • Maliro 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nyamuka! Lira mofuula usiku, pa nthawi yoyamba ulonda+ wam’mawa.

      Khuthula+ mtima wako pamaso+ pa Yehova ngati madzi.

      Pemphera utakweza manja+ ako kwa iye chifukwa cha ana ako,

      Amene akukomoka ndi njala m’misewu.+

  • Maliro 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Lilime la ana oyamwa lamamatira kummero chifukwa cha ludzu.+

      Ana apempha chakudya+ koma palibe amene akuwapatsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena