Maliro 4:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Wodzozedwa wa Yehova,+ amene ndi mpweya wotuluka mphuno mwathu,+ wagwidwa m’dzenje lawo lalikulu.+Ponena za ameneyu, ife tinati: “Tidzakhala mumthunzi wake+ pakati pa mitundu ya anthu.”+ Ezekieli 30:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 “Yehova wanena kuti, ‘Nawonso othandiza Iguputo adzaphedwa, ndipo mphamvu zimene amazinyadira zidzatha.’+ “‘Kuchokera ku Migidoli+ mpaka ku Seyene,+ anthu adzaphedwa ndi lupanga m’dzikolo,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa. Ezekieli 32:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 “‘Amenewa ndiwo anthu amene Farao adzawaone ndipo mtima wake udzakhala pansi poona khamu lake lonse.+ Farao ndi gulu lake lonse lankhondo adzakhala m’gulu la anthu ophedwa ndi lupanga,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.
20 Wodzozedwa wa Yehova,+ amene ndi mpweya wotuluka mphuno mwathu,+ wagwidwa m’dzenje lawo lalikulu.+Ponena za ameneyu, ife tinati: “Tidzakhala mumthunzi wake+ pakati pa mitundu ya anthu.”+
6 “Yehova wanena kuti, ‘Nawonso othandiza Iguputo adzaphedwa, ndipo mphamvu zimene amazinyadira zidzatha.’+ “‘Kuchokera ku Migidoli+ mpaka ku Seyene,+ anthu adzaphedwa ndi lupanga m’dzikolo,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.
31 “‘Amenewa ndiwo anthu amene Farao adzawaone ndipo mtima wake udzakhala pansi poona khamu lake lonse.+ Farao ndi gulu lake lonse lankhondo adzakhala m’gulu la anthu ophedwa ndi lupanga,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.