Salimo 109:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Iye anakonda kutemberera ena,+ mwakuti matemberero anabwera kwa iye.+Koma kudalitsa ena sikunali kumusangalatsa,+Moti madalitso anali patali ndi iye,+ Ezekieli 25:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 ‘Ine ndidzalanga Edomu kudzera mwa anthu anga Aisiraeli.+ Aisiraeliwo adzachitira Edomu mogwirizana ndi mkwiyo komanso ukali wanga, ndipo Aedomuwo adzadziwa mmene ndimalangira,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”’
17 Iye anakonda kutemberera ena,+ mwakuti matemberero anabwera kwa iye.+Koma kudalitsa ena sikunali kumusangalatsa,+Moti madalitso anali patali ndi iye,+ Ezekieli 25:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 ‘Ine ndidzalanga Edomu kudzera mwa anthu anga Aisiraeli.+ Aisiraeliwo adzachitira Edomu mogwirizana ndi mkwiyo komanso ukali wanga, ndipo Aedomuwo adzadziwa mmene ndimalangira,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”’
14 ‘Ine ndidzalanga Edomu kudzera mwa anthu anga Aisiraeli.+ Aisiraeliwo adzachitira Edomu mogwirizana ndi mkwiyo komanso ukali wanga, ndipo Aedomuwo adzadziwa mmene ndimalangira,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”’