Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 83:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iwo anena kuti: “Bwerani tiwafafanize kuti asakhalenso mtundu,+

      Ndi kuti dzina la Isiraeli lisakumbukikenso.”+

  • Ezekieli 36:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mawu amene Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena ndi akuti, ‘Ndithudi, ndidzadzudzula anthu otsala a mitundu ina ndiponso Edomu yense nditakwiya kwambiri.+ Ndidzadzudzula amene anatenga dziko langa kuti likhale lawo. Iwo analitenga akusangalala+ komanso kunyoza mumtima mwawo+ poona kuti atenga dzikolo ndi malo ake odyetserako ziweto.’”’+

  • Obadiya 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iwe sunayenera kulowa pachipata cha anthu anga pa tsiku limene anakumana ndi tsoka.+ Ndithu iweyo sunayenera kuyang’anitsitsa tsoka la m’bale wako pa tsiku limene anawonongedwa. Ndipo sunayeneranso kutambasula dzanja lako ndi kutenga chuma chake pa tsiku limene iye anakumana ndi tsoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena