Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 26:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Motero ndidzayendadi pakati panu ndi kukusonyezani kuti ine ndine Mulungu wanu,+ ndipo inu mudzakhala anthu anga.+

  • Ezekieli 11:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 kuti azidzatsatira malamulo anga, azidzasunga zigamulo zanga ndi kuzikwaniritsa.+ Iwo adzakhaladi anthu anga+ ndipo ine ndidzakhala Mulungu wawo.”’+

  • Ezekieli 36:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Inu mudzakhala m’dziko limene ndinapatsa makolo anu.+ Mudzakhala anthu anga ndipo ine ndidzakhala Mulungu wanu.’+

  • Ezekieli 43:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pamenepo Mulungu anandiuza kuti:

      “Iwe mwana wa munthu, malo awa ndi malo a mpando wanga wachifumu+ ndiponso poikapo mapazi anga.+ Ndidzakhala pamalo amenewa, pakati pa ana a Isiraeli mpaka kalekale.+ A nyumba ya Isiraeli ndi mafumu awo+ sadzaipitsanso dzina langa loyera+ ndi dama lawo komanso ndi mitembo+ ya mafumu awo.*

  • Hoseya 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamenepo ndidzamufesa ngati mbewu zanga padziko lapansi.+ Ndidzachitira chifundo amene sanasonyezedwe chifundo+ ndipo ndidzauza anthu amene si anthu anga kuti: “Inu ndinu anthu anga,”+ ndipo iwo adzayankha kuti: “Inu ndinu Mulungu wathu.”’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena