Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 93:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Zikumbutso zanu ndi zodalirika zedi.+

      Chiyero ndi choyenera nyumba yanu+ mpaka muyaya, inu Yehova.+

  • Ezekieli 40:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 M’masomphenya a Mulungu, iye ananditengera m’dziko la Isiraeli ndi kundikhazika paphiri lalitali kwambiri.+ Mbali ya kum’mwera paphiripo panali chinachake chooneka ngati mzinda.+

  • Ezekieli 42:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anayeza malo onsewo mbali zonse zinayi. Malo onsewo anali ndi mpanda+ wokwana mabango 500 m’litali ndi mabango 500 m’lifupi mwake.+ Mpandawo unali kusiyanitsa zinthu zopatulika ndi zinthu zodetsedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena