Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma nyama ya ng’ombeyo, chikopa chake ndi ndowe zake uzitenthe ndi moto kunja kwa msasa.+ Ng’ombeyo ndi nsembe yamachimo.

  • Levitiko 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma chikopa cha ng’ombeyo, nyama yake ndi ndowe zake anazitentha kunja kwa msasa,+ monga mmene Yehova analamulira Mose.

  • Aheberi 13:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti nyama zimene magazi ake, mkulu wa ansembe amalowa nawo m’malo oyera chifukwa cha machimo, amakazitentha kunja kwa msasa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena