Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 12:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Iwe mwana wa munthu, kodi mwambi umene anthu inu okhala m’dziko la Isiraeli mukunena+ wakuti, ‘Masiku akupita+ koma palibe masomphenya amene akwaniritsidwa,’+ umatanthauza chiyani?

  • 2 Petulo 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 amene azidzati:+ “Kukhalapo* kwake kolonjezedwa kuja kuli kuti?+ Taonani, kuchokera tsiku limene makolo athu anamwalira, zinthu zonse zikupitirirabe chimodzimodzi ngati mmene zakhalira kuyambira pa chiyambi cha chilengedwe.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena