Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Kuti pasapezeke wondikhadzulakhadzula ngati mmene mkango umachitira,+

      Pasapezeke wondikwatula popanda wondilanditsa.+

  • Nahumu 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kodi malo obisalamo mikango, phanga la mikango yamphamvu, malo amene mkango unali kuyenda ndi kulowa,+ malo amene munali mwana wa mkango, mmene mikango inali kukhala popanda woiwopsa, ali kuti?+

  • Zefaniya 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Akalonga ake anali mikango imene inali kubangula.+ Oweruza ake anali mimbulu yoyenda usiku imene sinatafune mafupa mpaka m’mawa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena