Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 16:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 “‘Mkulu wako amene akukhala kumanzere kwako ndiye Samariya+ ndi midzi yake yozungulira.+ Mng’ono wako, amene akukhala mbali ya kudzanja lako lamanja ndi Sodomu+ ndi midzi yake yozungulira.+

  • Amosi 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iwo amalumbira pa milungu yonama ya ku Samariya,*+ ya ku Dani,+ ndi ya ku Beere-seba.*+ Ndithu, anthu amenewa adzagwa ndipo sadzadzukanso.’”+

  • Mika 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Izi zichitika chifukwa cha kupanduka kwa Yakobo ndiponso chifukwa cha machimo a nyumba ya Isiraeli.+ Kodi wachititsa kupanduka kwa Yakobo ndani? Kodi si anthu a ku Samariya?+ Wachititsa ndani kuti Yuda akhale ndi malo okwezeka?+ Si anthu a ku Yerusalemu kodi?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena