Salimo 106:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Iwo anayamba kusakanikirana ndi mitundu ina,+Ndi kuyamba kuphunzira zochita zawo.+ Ezekieli 23:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 “Ohola anayamba kuchita uhule+ ngakhale kuti anali mkazi wanga. Anali kulakalaka kwambiri amuna amene ankakhumba kugona naye.+ Anali kulakalaka Asuri+ amene anali kukhala moyandikana naye.
5 “Ohola anayamba kuchita uhule+ ngakhale kuti anali mkazi wanga. Anali kulakalaka kwambiri amuna amene ankakhumba kugona naye.+ Anali kulakalaka Asuri+ amene anali kukhala moyandikana naye.