Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Komanso guwa lansembe limene linali ku Beteli+ ndi malo okwezeka amene Yerobowamu+ mwana wa Nebati amene anachimwitsa Isiraeli+ anamanga, ngakhale guwa lansembe limenelo ndi malo okwezekawo, mfumuyo inagumula. Kenako inatentha malo okwezekawo n’kuwaperapera mpaka kusanduka fumbi. Inatenthanso mzati wopatulika.

  • 2 Mafumu 23:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yosiya anachotsanso akachisi onse+ a m’malo okwezeka amene anali m’mizinda+ ya ku Samariya, amene mafumu+ a Isiraeli anamanga kuti akwiyitse Mulungu.+ Iye anawachitira zofanana ndi zonse zimene anachita ku Beteli.+

  • 2 Mbiri 31:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Atangomaliza kuchita zonsezi, Aisiraeli+ onse amene anali pamenepo anapita kumizinda ya Yuda+ n’kukaphwanya zipilala zopatulika,+ kukadula mizati yopatulika+ ndi kukagwetsa malo okwezeka+ ndi maguwa ansembe+ mu Yuda yense,+ mu Benjamini, mu Efuraimu+ ndi m’Manase+ mpaka kumaliza ntchitoyo. Atatero, ana onse a Isiraeli anabwerera kumizinda yawo, aliyense kumalo ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena