Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 15:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Panali pa nthawi imeneyi pamene Menahemu anachoka ku Tiriza n’kupita kukaukira mzinda wa Tifisa, n’kupha anthu onse amene anali mmenemo. Anawononganso dera lozungulira mzindawo chifukwa anthu ake sanamutsegulire chipata, ndipo akazi onse apakati a mumzindawo anawatumbula.+

  • Yeremiya 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti imfa yatilowera m’nyumba kudzera m’mawindo. Yalowa munsanja zathu zokhalamo kuti mumsewu musapezeke mwana aliyense ndiponso kuti anyamata asapezeke m’mabwalo a mzinda.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena