Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 48:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ife taona zimene Mulungu anachita monga mmene tinamvera,+

      Mumzinda wa Yehova wa makamu, mumzinda wa Mulungu wathu.+

      Mulungu adzakhazikitsa mzindawo mpaka kalekale.+ [Seʹlah.]

  • Yesaya 60:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “M’malo mokhala wosiyidwa mpaka kalekale ndi wodedwa, popanda aliyense wodutsa mwa iwe,+ ine ndidzakuika monga chinthu chonyaditsa mpaka kalekale, ndiponso chinthu chokondweretsa ku mibadwomibadwo.+

  • Amosi 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “‘Ine ndidzawabzala panthaka yawo ndipo sadzazulidwanso m’dziko limene ndawapatsa,’+ watero Yehova Mulungu wanu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena