Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma patapita masiku angapo, mtsinjewo unauma,+ chifukwa padziko lapansi sipanabwere mvula.

  • 1 Mafumu 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno Ahabu anauza Obadiya kuti: “Pita m’dzikoli, ukayendere akasupe onse a madzi ndi zigwa* zonse. Mwina tikhoza kupeza udzu wobiriwira+ woti tidyetse mahatchi ndi nyulu, kuti nyamazi zisapitirize kufa.”+

  • Yeremiya 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mawu amene Yehova anauza Yeremiya pa nkhani ya chilala+ ndi awa:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena