Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Ndipo pa tsiku limeneli, Yehova anatulutsa ana a Isiraeli malinga ndi makamu awo+ m’dziko la Iguputo.

  • Salimo 105:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Choncho Mulungu anatulutsa anthu ake m’dzikomo anthuwo akusangalala,+

      Anatulutsa osankhidwa ake akufuula mokondwera.+

  • Mika 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ine ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo,+ ndipo ndinakuwombolani m’nyumba ya akapolo.+ Ndinakutumizirani Mose, Aroni ndi Miriamu kuti akutsogolereni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena