Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 112:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Woipa adzaona zimenezi ndipo adzasautsika.+

      ש [Shin]

      Adzakukuta mano ndi kusungunuka.+

      ת [Taw]

      Chikhumbo cha anthu oipa chidzatha.+

  • Mateyu 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 pamene ana a ufumuwo+ adzaponyedwa kunja kumdima. Kumeneko adzalira ndi kukukuta mano.”+

  • Mateyu 25:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ponyani kapolo wopanda pake ameneyu kunja kumdima. Kumeneko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.’+

  • Luka 13:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kunjako n’kumene inu mudzalira ndi kukukuta mano,+ pamene mudzaona Abulahamu, Isaki ndi Yakobo, komanso aneneri onse ali mu ufumu wa Mulungu,+ koma inuyo atakukankhirani kunja.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena