Maliko 16:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Atalowa m’manda achikumbutsowo, anaona mnyamata atakhala pansi kudzanja lamanja, atavala mkanjo woyera, ndipo iwo anadabwa kwambiri.+ Luka 24:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Atathedwa nzeru ndi zimenezi, anangoona amuna awiri ovala zovala zonyezimira ataima pambali pawo.+ Machitidwe 1:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Mmene iwo anali kuyang’anitsitsa kuthambo pamene iye anali kukwera kumwamba,+ panaonekera amuna awiri ovala zoyera+ ataimirira pambali pawo. Chivumbulutso 10:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Kenako, ndinaona mngelo+ wina wamphamvu akutsika kuchokera kumwamba, atavala mtambo.+ Kumutu kwake kunali utawaleza, ndipo nkhope yake inali ngati dzuwa.+ Miyendo yake+ inali ngati mizati yamoto.
5 Atalowa m’manda achikumbutsowo, anaona mnyamata atakhala pansi kudzanja lamanja, atavala mkanjo woyera, ndipo iwo anadabwa kwambiri.+
10 Mmene iwo anali kuyang’anitsitsa kuthambo pamene iye anali kukwera kumwamba,+ panaonekera amuna awiri ovala zoyera+ ataimirira pambali pawo.
10 Kenako, ndinaona mngelo+ wina wamphamvu akutsika kuchokera kumwamba, atavala mtambo.+ Kumutu kwake kunali utawaleza, ndipo nkhope yake inali ngati dzuwa.+ Miyendo yake+ inali ngati mizati yamoto.