Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 11:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti zimene ndinalandira kwa Ambuye n’zimene inenso ndinakupatsirani, zakuti Ambuye Yesu, usiku+ umene anali kukaperekedwa anatenga mkate.

  • 2 Petulo 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 kuti mukumbukire mawu amene aneneri oyera ananena kale,+ ndi lamulo la Ambuye ndi Mpulumutsi wathu kudzera mwa atumwi anu.+

  • 1 Yohane 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Lamulo lake ndi lakuti, tikhale ndi chikhulupiriro m’dzina la Mwana wake Yesu Khristu+ ndiponso tizikondana,+ monga mmene iye anatilamulira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena