Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 17:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Ambuye, muchitire chifundo mwana wanga wamwamuna, chifukwa ndi wakhunyu ndipo akuvutika kwambiri. Amagwera pamoto kawirikawiri ndiponso amagwera m’madzi kawirikawiri.+

  • Maliko 1:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Chakumadzulo dzuwa litalowa, anthu anayamba kumubweretsera odwala onse+ ndi ogwidwa ziwanda,+

  • Machitidwe 5:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiponso anthu ambirimbiri ochokera m’mizinda yozungulira Yerusalemu anali kukhamukira kumeneko, atanyamula anthu odwala komanso amene mizimu yonyansa inali kuwazunza. Ndipo onsewo anali kuchiritsidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena