23 Kondwerani pa tsiku limenelo ndi kudumphadumpha, chifukwa mphoto yanu ndi yaikulu kumwamba, pakuti zomwezo ndi zimenenso makolo awo akale anachitira aneneri.+
41 Choncho atumwiwo anachoka pamaso pa Khoti Lalikulu la Ayuda, ali osangalala+ chifukwa chakuti Mulungu anawaona kuti ndi oyenera kuchitiridwa chipongwe chifukwa cha dzina la Yesu.+