Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 13:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 ndipo nthendayo ikuoneka yobiriwira mopitira ku chikasu kapena yofiirira pachovala kapena pachikopa, m’litali kapena m’lifupi mwa nsalu, kapena pachinthu chilichonse chopangidwa ndi chikopa, imeneyo ndi nthenda ya khate ndipo iyenera kusonyezedwa kwa wansembe.

  • Levitiko 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Ili likhale lamulo lokhudza wakhate+ pa tsiku limene adzam’bweretsa kwa wansembe kudzagamulidwa kuti ndi woyera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena