Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 17:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno anakumbatira mwanayo+ katatu ali pabedipo n’kufuulira Yehova kuti: “Inu Yehova Mulungu wanga, chonde chititsani kuti moyo+ wa mwanayu ubwerere mwa iye.”

  • Luka 8:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Koma iye anamugwira dzanja ndi kuitana kuti: “Mtsikana iwe, dzuka!”+

  • Yohane 11:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Atanena zimenezi, anafuula mokweza mawu kuti: “Lazaro, tuluka!”+

  • Machitidwe 9:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Koma Petulo anatulutsa anthu onse,+ ndiyeno anagwada pansi ndi kupemphera. Kenako anatembenukira mtembowo ndi kunena kuti: “Tabita, dzuka!” Pamenepo mayiyo anatsegula maso ake, ndipo mmene anaona Petulo, anadzuka n’kukhala tsonga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena