Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 ndipo anauza atumiki ake kuti: “Ameneyu ndi Yohane M’batizi. Anauka kwa akufa, ndipo n’chifukwa chake akuchita ntchito zamphamvu.”+

  • Maliko 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano izi zinamveka kwa Mfumu Herode,* chifukwa dzina la Yesu linamveka paliponse. Anthu anali kunena kuti: “Yohane m’batizi wauka kwa akufa, ndipo pa chifukwa chimenechi akuchita ntchito zamphamvu.”+

  • Maliko 8:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Iwo anamuyankha kuti: “Akumanena kuti Yohane M’batizi,+ ena akumati Eliya,+ koma ena akumati Mmodzi wa aneneri.”+

  • Luka 9:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Poyankha iwo anati: “Amati ndinu Yohane M’batizi. Koma ena amati ndinu Eliya. Enanso amati mmodzi wa aneneri akale wauka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena