Luka 3:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndiyeno khamu la anthu linali kumufunsa kuti: “Nanga tichite chiyani?”+ Machitidwe 16:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Kenako anawatulutsa kunja n’kunena kuti: “Mabwana inu, ndichite chiyani+ kuti ndipulumuke?”